Song parody of
Ponya
by Tha HP
Here's where you get creative! Use our cool song parody creator to make a totally new musical idea and lyrics for the Ponya song by Tha HP.
Simply click on any word to get rhyming words suggestion to use instead of the original ones. You may also remove or alter entire lines if needed — when you're done save your work and share it with our community — have fun!
Mwina ndikaponya
Mbedza yangayi sindikola
Mwinamwake sin'dziwa kuwedza
Ndeno chinachake chindiletsa
Mwina ndikaponya
Mwala wangawu sukawomba
Chinachake mtima chindilasa
Mwinamwake sin'dziwa kusaka
Mwina ndika--
Shatapu iwe ponya
Zoti sungathe sudziwa ponya
Usazibweze ndikukayikira ponya
Ungathe sungathe sungadziwe pokhapokha upange chisankho, ponya
Zoti sungathe sudziwa ponya
Usazibweze ndikukayikira ponya
Ungathe sungathe sungadziwe pokhapokha utaponya
Tonse timaopa
Mantha akabwera anthu timafooka
Mtima okayika umazatikoka
Kufuna kutichotsera zomwe timalota
(Koma osafooka)
Koma osafooka
Kutsogolo kuli kuwala kokhakokha
Bola chikayiko chako utachotsa
'Mwinamwake ine sin'ziwa kutosa,' mphwayiyo ndi tsoka
Khala chete ponya
Zoti sungathe sudziwa ponya
Usazibweze ndikukayikira ponya
Ungathe sungathe sungadziwe pokhapokha upange chisankho, ponya
Zoti sungathe sudziwa ponya
Usazibweze ndikukayikira ponya
Ungathe sungathe sungadziwe pokhapokha utaponya
Mwina ndikaponya
Mbedza yangayi sindikola
Mwinamwake sin'dziwa kuwedza
Ndeno chinachake chindiletsa
Mwina ndikaponya
Mwala wangawu sukawomba
Chinachake mtima chindilasa
Mwinamwake sin'dziwa kusaka
Mwina ndika--
Shatapu iwe ponya
Zoti sungathe sudziwa ponya
Usazibweze ndikukayikira ponya
Ungathe sungathe sungadziwe pokhapokha upange chisankho, ponya
Zoti sungathe sudziwa ponya
Usazibweze ndikukayikira ponya
Ungathe sungathe sungadziwe pokhapokha utaponya
Tonse timaopa
Mantha akabwera anthu timafooka
Mtima okayika umazatikoka
Kufuna kutichotsera zomwe timalota
(Koma osafooka)
Koma osafooka
Kutsogolo kuli kuwala kokhakokha
Bola chikayiko chako utachotsa
'Mwinamwake ine sin'ziwa kutosa,' mphwayiyo ndi tsoka
Khala chete ponya
Zoti sungathe sudziwa ponya
Usazibweze ndikukayikira ponya
Ungathe sungathe sungadziwe pokhapokha upange chisankho, ponya
Zoti sungathe sudziwa ponya
Usazibweze ndikukayikira ponya
Ungathe sungathe sungadziwe pokhapokha utaponya